Loto la mtsogoleri wa kale wa dziko lino malemu Bingu Wa Mutharika loti Malawi akhale ndi…
Category: Za Chichewa
CHASITSA DZAYE KUTI MZONDI AMANGIDWE
Posachedwapa takupasirani nkhani yoti yoti mzondi mkandawire wamangidwa ku karonga. Malingana ndi malipoti akuonetsa kuti ku…
Obwande kuchokera pa 12 March 2021
Mverani Obwande mu audio ili m’mwambayi, tipepese chifukwa chochedwerapo kukupatsirani obwande. Izi zidachitika chifukwa Cha zovuta…
NSANJE NORTH KWAFIKA MAGETSI, KWA CHAMBULUKA
Kunali Chimwemwe Ku Nsanje North, Mdera lotchedwa Chambuluka pamene a ESCOM pansi pa utsogoleri wa Dr…
CHAKWERA ALANDIRA KATEMERA WA COVID19
Nkhani ya Katemera wa covid19 yadzetsa manong’onong’o mdziko muno ponena kuti katemerayi ndioyipa mnthupi mwa munthu.…
A POLICE KU LILONGWE AMANGA TELALA PA MLANDU WOGWILIRA
A police amanga Raffick Issa wa zaka 29 kamba kogwilira mtsikana wa zaka 15, izi zatsimikizidwa…