MPUNGWEPUNGWE PAKATI PA MAJOR NDI MKAKA

A Alex Major yemwe ndi wachinyamata wa chipani cha MCP walembera kalata mlembi wamkulu wachipanichi a Eisenhower Mkaka kuti awabwenzeretse m’chipani mwansanga ndipo kupanda kutero akamang’ala ku bwalo la milandu.

Koma avant publications yapeza kuti a Mkaka sakuziwa chilichonse pa nkhaniyo kamba koti sanalandire chikalatati.

A mkaka sabata latha anachotsa a major mchipanichi kamba koti amachita zosokoneza komanso kulankhula zosakhala bwino za president wa dziko lino ndi ulamuliro wake.

www.avantmalawi.com

DR MWALE

Share this article

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *