A HENRY ZEMBERE AMWALIRA

olemba Dr mwale

Phungu wakale wa nyumba ya malamulo wa dera la Kumpoto kwa boma la Neno a Henry Zembere amwalira atadwala kwa nthawi yayitali matenda a Sugar komanso kuthamanga kwambiri kwa magazi (high blood pressure BP)
.
a Zembere   anakhalapo Phungu wa chipani Cha UDF  ku nyumba ya malamulo mu www.avantmalawi.com ulamuliro wa Dr Bakili Muluzi kuchokera mchaka cha 1994 mpaka  1999.
Malemuwo  amwalira ndi zaka 81 ndipo asiya ana 7.

Mwambo wa maliro uchitika mawa m’mudzi mwa Kaponda m’bomalo.

Share this article

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *